Onani zimene zilipo

Onani nkhani zake

4-G

Zocitika Zazikulu Paumoyo wa Yesu wa Padziko​—Utumiki Womaliza wa Yesu m’Yerusalemu (Mbali 1)

Zocitika Zazikulu Paumoyo wa Yesu wa Padziko​—Utumiki Womaliza wa Yesu m’Yerusalemu (Mbali 1)

NTHAWI

MALO

COCITIKA

MATEYU

MALIKO

LUKA

YOHANE

33, Nisani 8

Betaniya

Yesu afika masiku 6 Pasika asanayambe

     

11:55–12:1

Nisani 9

Betaniya

Mariya athila mafuta m’mutu wa Yesu ndi kumapazi ake

26:6-13

14:3-9

 

12:2-11

Betaniya-Betefage- Yerusalemu

Aloŵa mu Yerusalemu mwacisangalalo, atakwela bulu

21:1-11, 14-17

11:1-11

19:29-44

12:12-19

Nisani 10

Betaniya-Yerusalemu

Atembelela mtengo wa nkhuyu; ayeletsanso kacisi

21:18, 19; 21:12, 13

11:12-17

19:45, 46

 

Yerusalem Mkulu wansembe ndi alembi akonza ciwembu cofuna kupha Yesu

 

11:18, 19

19:47, 48

 

Yehova alankhula; Yesu anenelatu za imfa yake; kusakhulupilila kwa Ayuda kukwanilitsa ulosi wa Yesaya

     

12:20-50

Nisani 11

Betaniya-Yerusalemu

Phunzilo la mtengo wa mkuyu wofota

21:19-22

11:20-25

   

Yerusalemu, kacisi

Atsutsa ulamulilo wake; mafanizo a ana aŵili

21:23-32

11:27-33

20:1-8

 

Mafanizo: alimi akupha, phwando la cikwati

21:33–22:14

12:1-12

20:9-19

 

Ayankha mafunso onena za Mulungu ndi Kaisara, ciukililo, lamulo lalikulu

22:15-40

12:13-34

20:20-40

 

Afunsa khamu la anthu ngati Kristu ndi mwana wa Davide

22:41-46

12:35-37

20:41-44

 

Tsoka alembi ndi Afalisi

23:1-39

12:38-40

20:45-47

 

Aona copeleka ca mkazi wamasiye

 

12:41-44

21:1-4

 

Phili la Maolivi

Apeleka cizindikilo ca kubwela kwake kwa mtsogolo

24:1-51

13:1-37

21:5-38

 

Mafanizo: Anamwali 10, matalente, nkhosa ndi mbuzi

25:1-46

     

Nisani 12

Yerusalemu

Atsogoleli aciyuda akonza ciwembu cofuna kumupha

26:1-5

14:1, 2

22:1, 2

 

Yudasi alinganiza zom’peleka

26:14-16

14:10, 11

22:3-6

 

Nisani 13 (Cinai masana)

Mu Yerusalemu ndi capafupi

Akonzekela Pasika womaliza

26:17-19

14:12-16

22:7-13

 

Nisani 14

Yerusalemu

Akudya mgonelo ndi atumwi ake

26:20, 21

14:17, 18

22:14-18

 

Asambika mapazi a ophunzila ake

     

13:1-20