Mfundo za m'Mau a Mulungu

Mfundo za m’Mau a Mulungu

Pezani mayankho mʼBaibulo a mafunso 20 ofunika kwambili.

FUNSO 1

Kodi Mulungu ndani?

Zipembedzo zambili zimaphunzitsa kuti Mulungu ndi wosamvetsetseka kapena mphamvu cabe, koma Baibulo limanena zosiyana ndi zimenezi.

FUNSO 2

Mungaphunzile Bwanji za Mulungu?

kungoŵelenga Baibulo n’kokwanila?

FUNSO 3

Ndani analemba Baibulo?

Kodi ndi buku la nzelu za anthu kapena locokela kwa Mulungu?

FUNSO 4

Kodi Baibulo ndi Loona pankhani za Sayansi? ‵

Ngati Baibulo ndi locokela kwa Mulungu liyenela kukhala loona pankhani za sayansi.

FUNSO 5

Kodi m’Baibulo Muli uthenga Wotani?

Mavesi okwanila 10 amatipatsa cithunzi cokwanila ca uthenga wa m’Baibulo

FUNSO 6

Kodi Baibulo linalosela ciani za Mesiya?

Maulosi ambili anakwanilitsidwa pa Yesu

Funso 7

Kodi Baibulo linalosela ciani za nthawi yathu ino?

Kodi kuculuka kwa nkhondo, njala, kuphwanya malamulo, kuloŵa pansi kwa makhalidwe abwino kutanthauzanji?

FUNSO 8

Kodi Mulungu ndiye amacititsa kuti anthu azivutika?

Kodi Mulungu amatiyesa ndi mavuto?

FUNSO 9

N’cifukwa ciani anthu amavutika?

Ngati Mulungu si amene amacititsa mavuto, kodi ndani amawacititsa?

FUNSO 11

N’ciani Cimacitika Munthu Akafa?

Kodi imfa ndi njila yoloŵela ku moyo winawake?

FUNSO 13

Kodi Baibulo limakamba ciani za nchito?

Anthu ambili amaona kuti nchito ndi yotopetsa cakuti amangoigwila mokakamizika. Kodi izi ndi zimene Mulungu amafuna?

FUNSO 14

Cuma canu mungacisamalile bwanji??

Mfundo za nzelu za m’Baibulo zingakuthandize kulamulila cuma canu mmalo mwakuti cuma cizikulamulilani.

FUNSO 15

Mungacipeze bwanji cimwemwe?

Baibulo lili ndi mfundo zothandiza kupeza cimwemwe ndi kukhala okhutila.

FUNSO 16

Mungapilile bwanji nkhawa?

Mukapanikizika, Baibulo lingakuthandizeni.

FUNSO 17

Kodi Baibulo lingathandize bwanji banja lanu?

Phunzilani mmene Banja lanu lingakhalile malo osangalatsa ndi amtendele.

FUNSO 18

Mungayandikile bwanji Mulungu?

N’zotheka inuyo kukhala paubwenzi wabwino kwambili ndi Mulungu.

FUNSO 19

Kodi mabuku a m’Baibulo ali ndi uthenga wotani?

Phunzilani zambili zopezeka m’Baibulo.

FUNSO 20

Mungacite ciani kuti mupindule kwambili pamene muŵelenga baibulo?

Mosasamala kanthu ndi mbali iliyonse ya Baibulo imene mungaŵelenge, kupeza mayankho a mafunso anai kungakuthandizeni kupindula kwambili.