Onani zimene zilipo

Onani nkhani zake

FUNSO 15

Mungacipeze bwanji cimwemwe?

Mungacipeze bwanji cimwemwe?

“Ndi bwino kudya zamasamba koma pali cikondi, kusiyana ndi kudya nyama ya ng’ombe yamphongo yodyetsedwa bwino pali cidani.”

Miyambo 15:17

“Ine Yehova ndine Mulungu wanu, amene ndimakuphunzitsani kuti zinthu zikuyendeleni bwino, amene ndimakucititsani kuti muyende m’njila imene muyenela kuyendamo.”

Yesaya 48:17

“Odala ndi anthu amene amazindikila zosoŵa zao zauzimu, cifukwa ufumu wakumwamba ndi wao.”

Mateyu 5:3

“Uzikonda mnzako mmene umadzikondela wekha.”

Mateyu 22:39

“Zimene mukufuna kuti anthu akucitileni, inuyo muwacitile zomwezo.”

Luka 6:31

“Odala ndi amene akumva mau a Mulungu ndi kuwasunga!”

Luka 11:28

“Munthu atakhala ndi zoculuka cotani, moyo wake sucokela m’zinthu zimene ali nazo.”

Luka 12:15

“Conco, pokhala ndi cakudya, zovala ndi pogona, tikhale okhutila ndi zinthu zimenezi.”

1 Timoteyo 6:8

“Kupatsa kumabweletsa cimwemwe coculuka kuposa kulandila.”

Machitidwe 20:35