Khalani Wolimba!
YOSWA 1:9
KUM’MAŴA
8:40 Nyimbo Zamalimba
8:50 Nyimbo Na. 38 na Pemphelo
9:00 Yehova Ndiye Amatipatsa “Mphamvu ndi Nyonga”
9:15 Khalani Wolimba—Mangani Cikhulupililo Canu
9:30 Khalani Wolimba—Kangalikani pa Kulalikila, na Kuphunzitsa Ena
9:55 Nyimbo Na. 7 na Zilengezo
10:05 Kucoka pa Kufooka, Kukhala Wolimba!
10:35 Kudzipatulila na Ubatizo
11:05 Nyimbo Na. 79
KUMASANA
12:20 Nyimbo Zamalimba
12:30 Nyimbo Na. 102
12:35 Zocitika
12:45 Cidule ca Nsanja ya Mlonda
13:15 Yosiilana: Khalani Wolimba—Cilikizani Ucifumu wa Yehova . . .
Monga Wacicepele
Monga Okwatilana
13:45 Nyimbo Na. 126 na Zilengezo
13:55 “Limbani M’cikhulupililo, . . . Khalani Amphamvu”
14:55 Nyimbo Na. 2 na Pemphelo