Pezani Mayankho pa Mafunso Aaya
N’cifukwa ciani tiyenela kukhala na cidalilo popempha Yehova kuti atipatse kulimba mtima? (Sal. 138:3)
Kodi tingatengele bwanji kulimba mtima kwa atumiki a Mulungu a m’nthawi zakale? (Mac. 4:31)
Nanga tingakhale bwanji olimba mtima mu ulaliki? (1 Ates. 2:2)
Cimatithandiza n’ciani kukhalabe olimba mtima zinthu zikakhala zovuta? (1 Pet. 2:21-23)
Kodi kulimba mtima kwathu kwacikhristu kuli na madalitso anji? (Aheb. 10:35)