Mau oyamba
KODI TINGAPEZE KUTI MALANGIZO OTITHANDIZA KUKHALA NA UMOYO WACIMWEMWE?
Baibo imakamba kuti: “Wodala ndi munthu amene . . . amakondwela ndi cilamulo ca Yehova, ndipo amaŵelenga ndi kusinkhasinkha cilamulo cake usana ndi usiku.”—Salimo 1:1, 2.
Nkhani 7 zimenezi, zifotokoza mfundo zimene kwa nthawi yaitali zakhala zothandiza maningi kuti munthu akhale wacimwemwe.