Onani zimene zilipo

Onani nkhani zake

Mau oyamba

Mau oyamba

KODI BAIBO IKALI YOTHANDIZA MASIKU ANO?

Popeza kuti pali cidziŵitso cambili-mbili m’dziko lamakono, kodi Baibo ni yakale kwambili cakuti siingatithandize masiku ano? Baibo imakamba kuti:

“Malemba onse anauzilidwa ndi Mulungu, ndipo ndi opindulitsa.”—2 Timoteyo 3:16.

Kope ino ya Nsanja ya Mlonda ipeleka umboni woonetsa kuti Baibo ingatithandize m’mbali zonse za umoyo wathu.