NSANJA YA MLONDA—YOPHUNZILA February 2016
Magaziniyi ili ndi nkhani zophunzila mlungu wa April 4 mpaka May 1, 2016.
Yehova Anamucha kuti “Bwenzi Langa”
Kodi mungakonde kukhala bwenzi la Yehova? Phunzilani citsanzo ca Abulahamu kuti muone zimene mungacite.
Tengelani Citsanzo ca Mabwenzi Apamtima a Yehova
Kodi n’ciani cinathandiza Rute, Hezekiya, ndi Mariya kukhala pa ubwenzi wolimba ndi Mulungu?
Khalani Wokhulupilika kwa Yehova
Citsanzo ca Yonatani cingatithandize kukhala wokhulupilika kwa Yehova pa zocitika zinai zovuta.
Tengelani Citsanzo ca Atumiki Okhulupilika a Yehova
Kodi Davide, Yonatani, Natani, ndi Husai anaonetsa bwanji kuti kukhala wokhulupilika kwa Yehova ndiye cinthu coyamba pa umoyo wao?
MBILI YANGA
Yehova Wandidalitsa mu Utumiki Wake
Corwin Robison anatumikila Mulungu mokhulupilika kwa zaka 73, kuphatikizapo zaka zoposa 60 zimene anatumikila pa Beteli ku United States
Pitilizani Kutumikila Yehova Mwacimwemwe
Kusinkhasinkha mfundo zitatu zofunika kungakuthandizeni kukhalabe ndi cimwemwe.