NSANJA YA MLONDA—YOPHUNZILA August 2024
Magazini ino ili na nkhani zophunzila mu mlungu wa October 7–November 10, 2024.
NKHANI YOPHUNZILA 31
Zimene Yehova Anacita Kuti Apulumutse Anthu ku Ucimo
Yophunzila mu mlungu wa October 7-13, 2024.
Mafunso Ocokela Kwa Oŵelenga
Kodi kuika munthu cizindikilo kofotokozedwa pa 2 Atesalonika 3:14, kuyenela kucitika na akulu kapena wofalitsa aliyense payekha mumpingo?
NKHANI YOPHUNZILA 32
Yehova Amafuna Kuti Anthu Onse Alape
Yophunzila mu mlungu wa October 14-20, 2024.
NKHANI YOPHUNZILA 33
Mmene Mpingo Umaonetsela Maganizo a Yehova Kwa Munthu Amene Wacita Chimo
Yophunzila mu mlungu wa October 21-27, 2024.
NKHANI YOPHUNZILA 34
Mmene Akulu Amaonetsela Cikondi na Cifundo Kwa Munthu Wocita Chimo
Yophunzila mu mlungu wa October 28–November 3, 2024.
NKHANI YOPHUNZILA 35
Mmene Akulu Angathandizile Amene Anacotsedwa Mumpingo
Yophunzila mu mlungu wa November 4-10, 2024.
Cidziŵitso Kwa Oŵelenga
M’magazini ino, muli mpambo wa nkhani zophunzila zomwe zidzaonetsa mmene Yehova amaonela aja amene anacita chimo komanso mmene amawathandizila. Tidzaonanso mmene tingatengele khalidwe lake lacikondi na cifundo.