Onani zimene zilipo

Onani nkhani zake

Mlozela Nkhani wa Magazini a 2022 a Nsanja ya Mlonda na Galamuka!

Mlozela Nkhani wa Magazini a 2022 a Nsanja ya Mlonda na Galamuka!

Taonetsa kope yake imene mwacokela nkhaniyo

NSANJA YA MLONDA YOPHUNZILA

KODI MUDZIŴA?

  • Kodi anthu ochulidwa m’Baibo anali kudziŵa bwanji poyambila caka kapena mwezi? June

  • Kodi Aroma anali kulola munthu wopacikidwa pa mtengo, monga Yesu, kuti mtembo wake uikidwe m’manda? June

  • Kodi Moredekai analikodi? Nov.

  • N’cifukwa ciani Aisiraeli kalelo anali kupeleka malipilo a ukwati? Feb.

  • N’cifukwa ciani njiŵa komanso ana a nkhunda zinali kulandilidwa monga nsembe? Feb.

MAFUNSO OCOKELA KWA OŴELENGA

  • Kodi Baibo imati ciyani pa nkhani ya kucita malumbilo? Apr.

  • Kodi Davide ‘anamvelela bwanji cifundo’ Mefiboseti, koma pambuyo pake anapeleka Mefiboseti kuti akaphedwe? (2 Sam. 21:7-9), Mar.

  • Kodi Davide anali kuganiza kuti sadzamwalila polemba kuti adzatamanda dzina la Mulungu “mpaka muyaya”? (Sal. 61:8), Dec.

  • Kodi mtumwi Paulo anatanthauza ciyani pamene anati iye ni “khanda lobadwa masiku asanakwane”? (1 Akor. 15:8), Sept.

  • Kodi Yesu anatanthauza ciyani pokamba kuti: “Musaganize kuti ndinabweletsa mtendele”? (Mat. 10:34, 35), July

  • Mmene mpingo uyenela kuonela ukwati wakalewo ndiponso ukwati watsopanowo ngati Mkhristu si womasuka mwa Malemba, Apr.

  • Ndani adzaukitsidwa pano padziko lapansi? Nanga ciukitso cawo cidzakhala cotani? Sept.

MBILI YANGA

  • “N’nakwanilitsa Colinga Canga Cotumikila Yehova” (D. van Marl), Nov.

  • N’nalola Yehova Kunitsogolela Njila (K. Eaton), July

  • N’napeza Cinthu Cabwino Kuposa Kukhala Dokotala (R. Ruhlmann), Feb.

  • Nakhala Nikusangalala Kuphunzila za Yehova na Kuphunzitsako Ena (L. Weaver, Jr.), Sept.

MBONI ZA YEHOVA

  • 1922—Zaka 100 Zapitazo, Oct.

NKHANI ZOPHUNZILA

  • Anthu a Yehova Amakonda Cilungamo, Aug.

  • Buku la Chivumbulutso—Cimene Cidzacitikila Adani a Mulungu, May

  • Buku la Chivumbulutso—Mmene Likukhudzila Tsogolo Lanu, May

  • Buku la Chivumbulutso—Mmene Limakukhudzilani, May

  • Cifukwa Cake Timapezeka pa Cikumbutso, Jan.

  • Cikondi ca Yehova Cimatithandiza Kugonjetsa Mantha, June

  • Inu Acicepele—Pitanibe Patsogolo Pambuyo pa Ubatizo, Aug.

  • Inu Akulu—Pitilizani Kutsanzila Mtumwi Paulo, Mar.

  • Inu Anakubala—Phunzilani ku Citsanzo ca Yunike, Apr.

  • Inu Makolo—Thandizani Ana Anu Kukonda Yehova, May

  • Khalanibe Oganiza Bwino Kukhulupilika Kwanu Kukayesedwa, Nov.

  • Kodi Dzina Lanu Lilimo “M’buku la Moyo”? Sept.

  • Kodi Mumakhulupilila Mmene Yehova Amacitila Zinthu? Feb.

  • Kodi Mumatha Kuona Zimene Zekariya Anaona? Mar.

  • Kodi Ndinu “Citsanzo . . . M’kalankhulidwe”? Apr.

  • Kodi Uphungu Wanu ‘Umasangalatsa Mtima’? Feb.

  • Kodi Yehova Amatithandiza Bwanji Kupilila Mwacimwemwe? Nov.

  • Kulambila Koona Kudzawonjezela Cimwemwe Canu, Mar.

  • ‘Kuthandiza Anthu Ambili Kukhala Olungama,’ Sept.

  • Maso a Yehova Ali pa Anthu Ake, Aug.

  • Mmene Mungadziikile Zolinga Zauzimu na Kuzikwanilitsa, Apr.

  • Mmene Yehova Amatithandizila Kugwila Nchito Yolalikila, Nov.

  • Mukhoza Kucipeza Cimwemwe Ceniceni, Oct.

  • Musalole Ciliconse Kukulekanitsani na Yehova, Nov.

  • “Muzigwilitsa Nchito Bwino Nthawi Yanu,” Jan.

  • ‘Mvela Mawu a Anthu Anzelu,’ Feb.

  • N’zotheka Kudzakhala na Moyo Kwamuyaya, Dec.

  • N’zotheka Kuti Muziwadalila Abale Anu, Sept.

  • N’zotheka ‘Kuvula Umunthu Wakale,’ Mar.

  • Nzelu Yeniyeni Imafuula, Oct.

  • Nzelu Zothandiza pa Umoyo Wathu, May

  • “Odala ndi Anthu Osalakwitsa Kanthu” kwa Yehova, Oct.

  • “Ofuna-funa Yehova Sadzasoŵa Ciliconse Cabwino,” Jan.

  • Onetsani Kuti Ndinu Wodalilika, Sept.

  • Pezani Cimwemwe Popatsa Yehova Zabwino Zimene Mungathe Pacanu, Apr.

  • Pezani Mtendele pa Nthawi ya Mavuto, Dec.

  • Phunzilani Kwa Mng’ono Wake wa Yesu, Jan.

  • Pitilizani “Kulimbikitsana,” Aug.

  • Pitilizani Kulimbitsa Ciyembekezo Canu, Oct.

  • Pitilizani Kuvala “Umunthu Watsopano” Pambuyo pa Ubatizo, Mar.

  • Tengelani Citsanzo ca Yesu Cotumikila Ena, Feb.

  • Thandizani Ena Kupilila pa Nthawi Zovuta, Dec.

  • Tiyeni Tim’thandizile Yesu Monga Wotiyang’anila, July

  • Tiziyamikila Mwayi Wathu wa Pemphelo, July

  • “Udzakhala Ndi Ine m’Paradaiso,” Dec.

  • Ufumu wa Mulungu Ukulamulila! July

  • Ulosi Wamakedzana Umene Umakukhudzani, July

  • Yehova Amadalitsa Amene Amakhululukila Anzawo, June

  • Yehova Ni Wokonzeka Kukhululuka, June

  • “Yembekezela Yehova,” June

  • ‘Yendanibe M’coonadi,’ Aug.

  • Yesu Anagwetsa Misozi—Tiphunzilapo Ciani? Jan.

UMOYO NA MAKHALIDWE ACIKHRISTU

  • Kodi Ndinu Wokonzeka ‘Kukalandila Dziko Lapansi’? Dec.

  • Lolani Kuti “Lamulo la Kukoma Mtima Kosatha” Lizikutsogolelani, June

  • Mabisiketi a Tiagalu (ulaliki wa kasitandi), Apr.

  • Mmene Tingathanilane Nazo Nkhawa, Apr.

  • N’cifukwa Ciyani Ife Sitimenya Nkhondo Ngati Aisiraeli Akale? Oct.

NSANJA YA OLONDA YOGAŴILA

  • Kodi N’zotheka Kuthetsa Chidani? (Chichewa) Na. 1

GALAMUKANI!

  • Kodi Mungatani Kuti Mupirire Mavuto a M’Dzikoli? (Chichewa) Na. 1