Mfundo Zokhudza Buku la Esitere
Mfundo zokuthandizani kudziŵa mwamsanga zocitika m’nthawi ya Esitere ndi ubwino wa buku limeneli. Bukuli lionetsa mmene Esitere anacitila zinthu molimba mtima kuti ateteze anthu a Mulungu.
Mfundo zokuthandizani kudziŵa mwamsanga zocitika m’nthawi ya Esitere ndi ubwino wa buku limeneli. Bukuli lionetsa mmene Esitere anacitila zinthu molimba mtima kuti ateteze anthu a Mulungu.