Phunzilani kwa Mabwenzi a Yehova

Phunzilani kwa anthu osiyanasiyana ochulidwa m’Baibulo amene anakhala mabwenzi a Yehova!

Yeremiya

Kodi mungaphunzile ciyani kwa Yeremiya amene anali bwenzi la Yehova pa nkhani ya kukhala wolimba mtima?

Hananiya, Misayeli, ndi Azariya

Kodi mungakhale omvela monga mabwenzi a Yehova awa, Hananiya, Misayeli, ndi Azariya?

Pepani, palibe mawu olingana amene mwasankha.