Onani zimene zilipo

Onani nkhani zake

NYIMBO 153

Nilimbitseni Mtima

Nilimbitseni Mtima

(2 Mafumu 6:16)

  1. 1. Navutika mtima​—

    Nasoŵa cocita.

    Olo zinthu zinivute;

    Mumanithandiza.

    Moyo ungavute,

    Koma nimadziŵa:

    Ndimwe wokhulupilika;

    Mudzaniteteza.

    (KOLASI)

    Yehova, nithandizeni

    Kuti niziona.

    Tilidi ambili kuposa

    Olimbana nafe.

    Conde, n’thandizeni

    Kuti nipilile.

    Nilimbitseni mtima,

    Simungalephele.

  2. 2. Ndine cabe munthu.

    Nimacita mantha.

    Ndimwe pothaŵila panga;

    Simumalephela.

    Munipatse mphamvu,

    Kuti nisayope.

    Ine nidzapililabe​—

    Kufikila imfa.

    (KOLASI)

    Yehova, nithandizeni

    Kuti niziona.

    Tilidi ambili kuposa

    Olimbana nafe.

    Conde, n’thandizeni

    Kuti nipilile.

    Nilimbitseni mtima,

    Simungalephele.

    (KOLASI)

    Yehova, nithandizeni

    Kuti niziona.

    Tilidi ambili kuposa

    Olimbana nafe.

    Conde, n’thandizeni

    Kuti nipilile.

    Nilimbitseni mtima,

    Simungalephele.

    Nilimbitseni mtima,

    Simungalephele.