NYIMBO 155
Cimwemwe Cathu Camuyaya
(Salimo 16:11)
1. Kumwamba kuli nyenyezi
ndipo ziwala.
Munakongoletsa usana
na usiku.
Manja anu anapanga
zinthu zonse mukondwela
Mukaziona.
(KOLASI)
Cilengedwe canu M’lungu
Na uthenga wa Ufumu
Zimatikondweletsa.
Cikondi canu cosatha
Ndiye cuma camuyaya.
Ndimwe cimwemwe cathu.
Inde, ca muyaya.
2. Yehova tili na zonse
zosangalatsa—
Zonse tiona na maso,
zikhudza mtima.
Mwatipatsa umuyaya
Mumitima yathu,
Na cimwemwe cosatha.
(KOLASI)
Cilengedwe canu M’lungu
Na uthenga wa Ufumu
Zimatikondweletsa.
Cikondi canu cosatha
Ndiye cuma camuyaya.
Ndimwe cimwemwe cathu.
Inde, ca muyaya.
(BILIJI)
Munapeleka Yesu
Kuti atifele
Sitikanapeza cimwemwe
Popanda nsembe yake.
(KOLASI)
Cilengedwe canu M’lungu
Na uthenga wa Ufumu,
Zimatikondweletsa.
Cikondi canu cosatha
Ndiye cuma camuyaya.
Ndimwe cimwemwe cathu
Inde, ca muyaya.
(KOLASI)
Cilengedwe canu M’lungu
Na uthenga wa Ufumu
Zimatikondweletsa
Cikondi canu cosatha
Ndiye cuma camuyaya
Ndimwe cimwemwe cathu
Inde, ca muyaya.
(Onaninso Sal. 37:4; 1 Akor. 15:28.)