Mphamvu Yoposa Yanga
Daunilodi:
1. Nthawi zonse maganizo
Osautsa akaculuka,
Nimapemphela podziwa kuti
Yehova
Anithandiza.
(MWANA WA KOLASI)
Nipempha
Munipatse mzimu wanu.
(KOLASI)
Mwa mzimu wanu
Ningathe kuuluka inde m’mwamba.
Monga ciwombankhanga couluka,
Sin’dzafoka, nidzalimba.
Mwa mzimu wanu M’lungu.
2. Citonthozo canu M’lungu
Canipatsa mphamvu kuti nithe
Kuthandiza ena kuona
Cikondi canu cosasintha.
(MWANA WA KOLASI)
Nipempha
Munipatse mzimu wanu.
(KOLASI)
Mwa mzimu wanu
Ningathe kuuluka inde m’mwamba.
Monga ciwombankhanga couluka,
Sin’dzafoka, nidzalimba.
Mwa mzimu wanu M’lungu.
(KOLASI)
Mwa mzimu wanu
Ningathe kuuluka inde m’mwamba.
Monga ciwombankhanga couluka,
Sin’dzafoka, nidzalimba.
Mwa mzimu wanu M’lungu,
Mwa mzimu wanu M’lungu,
Mwa mzimu wanu M’lungu.