Kukaona Malo pa Beteli
Tikuitanani kuti mudzaone maofesi athu a nthambi, amene timayacha kuti Beteli. Maofesi ena a nthambi ali na ma miziyamu yakuti munthu akhoza kudzionela yekha zinthu popanda wina kumutsogolela.
Kuyambilanso Kukayendela Maofesi a Nthambi: Pa June 1, 2023, m'maiko ambili tinayambilanso kulola anthu kukayendela maofesi athu a nthambi. Kuti mumve zambili, funsilani ku ofesi ya nthambi imene mufuna kukayendela. Koma conde, osapitako ngati munapezeka na COVID-19, ngati muli na cimfine, kapena ngati caposacedwa munakhalako pafupi na munthu wodwala COVID-19.
Côte d’Ivoire
Rue J-58 - Lot 1758
Deux-Plateaux
3ème tranche, Vallon
ABIDJAN
CÔTE D’IVOIRE
+225 2241-3606
Kuona Malo
Pa Mande mpaka pa Cisanu
14:00hrs mpaka 16:00hrs
Nthawi yoona malo: Ola limodzi
Zimene Timacita
Timamasulila mabuku ofotokoza Baibulo m’Ciabeyi, Ciatiyi, Cibole, Cibete, Cigulo, Cigwele Cisenufo ndi Ciyakoba. Ndiponso timaika pa ma CD tumabuku ndi maseŵelo omvetsela m’zinenelo zambili.