Onani zimene zilipo

Kukaona Malo pa Beteli

Tikuitanani kuti mudzaone maofesi athu a nthambi, amene timayacha kuti Beteli. Maofesi ena a nthambi ali na ma miziyamu yakuti munthu akhoza kudzionela yekha zinthu popanda wina kumutsogolela.

Kuyambilanso Kukayendela Maofesi a Nthambi: Pa June 1, 2023, m'maiko ambili tinayambilanso kulola anthu kukayendela maofesi athu a nthambi. Kuti mumve zambili, funsilani ku ofesi ya nthambi imene mufuna kukayendela. Koma conde, osapitako ngati munapezeka na COVID-19, ngati muli na cimfine, kapena ngati caposacedwa munakhalako pafupi na munthu wodwala COVID-19.

Ghana

Nungua Police Checkpoint

Hse. No. J 348/4

Tema Beach Road

Nungua

ACCRA

GHANA

+233 30-701-0110

+233 30-2712-456

+233 30-2712-457

+233 30-2712-458

Kuona Malo

Pa Mande mpaka pa Cisanu

8:00hrs mpaka 11:00hrs ndi 13:00hrs mpaka 16:00hrs.

Nthawi yoona malo: Ola limodzi

Zimene Timacita

Timamasulila mabuku ofotokoza Baibulo m’Citwi, Ciewe, Ciga, Cidangime, Cinzema, Cifrafra, ndi Cidagaare. Ndipo timapanga ma CD a zofalitsa ndi mavidiyo m’Citwi, Ciewe, ndi m’Ciga. Timamanga Nyumba za Ufumu 60 caka ciliconse pa avaleji ndipo timatumiza mabuku olemela matani mahandiledi ambili m’dzikoli.

Tengani kapepala koonetsa malo.