Russia
Akuluakulu a Boma ku Russia Anathokoza Mwapadera a Mboni za Yehova Kuphatikizapo Nzika ya ku Denmark Yomwe ili M’ndende
Akuluakulu mumzinda wa Oryol anathokoza a Mboni za Yehova kuphatikizapo nzika ina ya ku Denmark yomwe ili m’ndende. Iwo anathokoza Amboniwo chifukwa chogwira nawo ntchito yoyeretsa mumzindawo yomwe imachitika chaka chilichonse.
A Mboni za Yehova Ochokera M’mayiko Osiyanasiyana Analimbikitsa Abale Awo a ku Russia pa Nthawi Yozenga Mlandu wa Apilo
Bungwe Lolamulira linatumiza abale ochokera m’mayiko osiyanasiyana kupita ku Moscow.
Vidiyo Yosonyeza Apolisi ku Russia Akusokoneza Misonkhano ya Mboni za Yehova
Vidiyo yomwe bungwe lina lofalitsa nkhani ku Russia linatulutsa inasonyeza apolisi a Federal Security Service omwe anali ndi zida akusokoneza misonkhano imene a Mboni za Yehova ankapanga mumzinda wa Oryol ku Russia.
Vidiyo Yosonyeza Apolisi ku Russia Akusokoneza Misonkhano ya Mboni za Yehova
Pa 25 May 2017, apolisi a Federal Security Service (FSB) omwe anali ndi zida anasokoneza misonkhano imene a Mboni za Yehova ankachita mwamtendere mumzinda wa Oryol ku Russia.
A Mboni za Yehova Padziko Lonse Akulimbikitsidwa Kulemba Makalata Opempha Kuti Boma la Russia Lisaletse Ntchito Yawo M’dzikolo
Boma la Russia laopseza kuti liletsa ntchito ya Mboni za Yehova m’dzikolo. Choncho a Mboni za Yehova padziko lonse aganiza zolemba makalata opita ku boma la Russia ndiponso kwa akuluakulu a Khoti Lalikulu m’dzikolo. Pali malangizo omwe angathandize aliyense amene akufuna kulemba nawo makalatawa.