October 16-22

YOBU 6-7

October 16-22
  • Nyimbo Na. 33 ndi Pemphero

  • Mawu Oyamba (1 min.)

CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU

  • Moyo Ukafika Povuta”: (10 min.)

  • Mfundo Zothandiza: (10 min.)

    • Yob 6:29—N’chiyani chingatithandize kuti tipewe kuweruza molakwika abale athu? (w20.04 16:10)

    • Pa kuwerenga Baibulo kwa mlungu uno, kodi mwapeza mfundo ziti zokhudza Yehova, utumiki kapena zinthu zina?

  • Kuwerenga Baibulo: (4 min.) Yob 6:​1-13 (th phunziro 2)

KUPHUNZITSA MWALUSO MU UTUMIKI

MOYO WATHU WACHIKHRISTU