October 2-8 YOBU 1-3 YAMBANI October 2-8 Pepani, zalephereka. Koperani Vidiyoyi Onetsani Kaonekedwe ka Mawu Bisani Kaonekedwe ka Mawu Nyimbo Na. 141 ndi Pemphero Mawu Oyamba (1 min.) CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU “Pitirizani Kusonyeza Kuti Mumakonda Kwambiri Yehova”: (10 min.) Mfundo Zothandiza: (10 min.) Yob 1:10—Kodi lembali likutithandiza bwanji kumvetsa mawu a Yesu opezeka pa lemba la Mateyu 27:46? (w21.04 15:9) Yankho Pa kuwerenga Baibulo kwa mlungu uno, kodi mwapeza mfundo ziti zokhudza Yehova, utumiki kapena zinthu zina? Yankho Kuwerenga Baibulo: (4 min.) Yob 3:1-15 (th phunziro 12) KUPHUNZITSA MWALUSO MU UTUMIKI Ulendo Woyamba: (3 min.) Yambani ndi nkhani imene ili mu chitsanzo cha ulendo woyamba. Kenako mufotokozereni za webusaiti yathu ya jw.org, ndipo mugawireni khadi lodziwitsa anthu za webusaitiyi. (th phunziro 9) Ulendo Wobwereza: (4 min.) Yambani ndi nkhani imene ili mu chitsanzo cha ulendo wobwereza. Yerekezerani kumuonetsa vidiyo yakuti N’chifukwa Chiyani Tiyenera Kuphunzira Baibulo?, kenako kambiranani naye mfundo za muvidiyoyi. (th phunziro 20) Nkhani: (5 min.) w22.01 2:11-14—Mutu: Tiziphunzitsa Mogwira Mtima Ngati Yakobo—Tizipereka Malangizo Mosapita M’mbali Komanso Tizikhala Odzichepetsa. (th phunziro 18) MOYO WATHU WACHIKHRISTU Nyimbo Na. 21 Ndinkaganiza Ngati Ndili Ndi Chilichonse: (10 min.) Nkhani yokambirana. Onerani vidiyoyi. Kenako funsani mafunso otsatirawa: N’chifukwa chiyani M’bale Birdwell ankaganiza kuti anali ndi chilichonse? Yankho Kodi kuganizira mfundo ya pa lemba la Mateyu 6:33 kunathandiza bwanji m’baleyu? Yankho Kodi mwaphunzirapo chiyani pa chitsanzo cha banja la a Birdwell? Yankho “Muzigwiritsa Ntchito Tsamba Loyamba la JW.ORG Mukakhala mu Utumiki”: (5 min.) Nkhani yokambirana. Phunziro la Baibulo la Mpingo: (30 min.) lff phunziro 51 Mawu Omaliza (3 min.) Nyimbo Na. 102 ndi Pemphero Yam'mbuyo Yotsatira Sindikizani Patsani ena Patsani ena October 2-8 UTUMIKI KOMANSO MOYO WATHU WACHIKHRISTU–NDANDANDA YA MISONKHANO Ndandanda ya Msonkhano wa Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu ya October 2-8, 2023 Chinenero Chamanja cha ku Malawi Ndandanda ya Msonkhano wa Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu ya October 2-8, 2023 https://cms-imgp.jw-cdn.org/img/p/202023331/univ/art/202023331_univ_sqr_xl.jpg mwb23.9 12