October 9-15 YOBU 4-5 YAMBANI October 9-15 Pepani, zalephereka. Koperani Vidiyoyi Onetsani Kaonekedwe ka Mawu Bisani Kaonekedwe ka Mawu Nyimbo Na. 121 ndi Pemphero Mawu Oyamba (1 min.) CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU “Samalani ndi Nkhani Zabodza”: (10 min.) Mfundo Zothandiza: (10 min.) Yob 4:4—Kodi Yobu anapereka chitsanzo chabwino chiti kwa Akhristu masiku ano? (w03-CN 5/15 22:5-6) Yankho Pa kuwerenga Baibulo kwa mlungu uno, kodi mwapeza mfundo ziti zokhudza Yehova, utumiki kapena zinthu zina? Yankho Kuwerenga Baibulo: (4 min.) Yob 5:1-12 (th phunziro 10) KUPHUNZITSA MWALUSO MU UTUMIKI Ulendo Woyamba: (2 min.) Gwiritsani ntchito nkhani imene ili mu chitsanzo cha ulendo woyamba. (th phunziro 4) Ulendo Wobwereza: (5 min.) Yambani ndi nkhani imene ili mu chitsanzo cha ulendo wobwereza. Musonyezeni mmene angapezere zinthu zosiyanasiyana pa jw.org. (th phunziro 15) Phunziro la Baibulo: (5 min.) lff phunziro 16 mfundo 5 (th phunziro 16) MOYO WATHU WACHIKHRISTU Nyimbo Na. 78 Zofunika Pampingo: (15 min.) Phunziro la Baibulo la Mpingo: (30 min.) lff phunziro 52 Mawu Omaliza (3 min.) Nyimbo Na. 29 ndi Pemphero Yam'mbuyo Yotsatira Sindikizani Patsani ena Patsani ena October 9-15 UTUMIKI KOMANSO MOYO WATHU WACHIKHRISTU–NDANDANDA YA MISONKHANO Ndandanda ya Msonkhano wa Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu ya October 9-15, 2023 Chinenero Chamanja cha ku Malawi Ndandanda ya Msonkhano wa Utumiki Komanso Moyo Wathu Wachikhristu ya October 9-15, 2023 https://cms-imgp.jw-cdn.org/img/p/202023334/univ/art/202023334_univ_sqr_xl.jpg mwb23.9 15