CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU Samalani ndi Nkhani Zabodza YAMBANI Samalani ndi Nkhani Zabodza Pepani, zalephereka. Koperani Vidiyoyi Onetsani Kaonekedwe ka Mawu Bisani Kaonekedwe ka Mawu Zimene Elifazi ankanena zinkaoneka ngati zoona chifukwa anali wamkulu komanso wanzeru (Yob 4:1; it-1 713:11) Ziwanda zinamutsogolera kuti akapereke uthenga wofooketsa kwa Yobu (Yob 4:14-16; w05-CN 9/15 26:2) Zina mwa zomwe Elifazi ananena zinali zoona, koma anazigwiritsa ntchito molakwika (Yob 4:19; w10-CN 2/15 19:5-6) Dziko la Satanali limafalitsa nkhani zabodza zowononga. DZIFUNSENI KUTI, ‘Kodi ndimapeza nthawi yoti nditsimikizire kaye ngati nkhani zimene ndikumva kapena kuwerenga zilidi zoona?’—mrt 32 ¶13-17 Yam'mbuyo Yotsatira Sindikizani Patsani ena Patsani ena Samalani ndi Nkhani Zabodza UTUMIKI KOMANSO MOYO WATHU WACHIKHRISTU–NDANDANDA YA MISONKHANO Samalani ndi Nkhani Zabodza Chinenero Chamanja cha ku Malawi Samalani ndi Nkhani Zabodza https://cms-imgp.jw-cdn.org/img/p/202023335/univ/art/202023335_univ_sqr_xl.jpg mwb23.9 16