CHUMA CHOPEZEKA M’MAWU A MULUNGU Zimene Tikuphunzira pa Nkhani ya Kulankhulana Bwino YAMBANI Zimene Tikuphunzira pa Nkhani ya Kulankhulana Bwino Pepani, zalephereka. Koperani Vidiyoyi Onetsani Kaonekedwe ka Mawu Bisani Kaonekedwe ka Mawu Esitere anayembekezera nthawi yabwino kuti alankhule (Est 7:2; ia 16:15-16) Analankhula mwanzeru komanso mwaulemu (Est 7:3; ia 16:17) Analankhula momveka bwino ndi moona mtima (Est 7:4; ia 16:18-19) DZIFUNSENI KUTI, ‘Kodi ndingatsanzire bwanji Esitere ndikamalankhula ndi anthu a m’banja langa?’ Yam'mbuyo Yotsatira Sindikizani Patsani ena Patsani ena Zimene Tikuphunzira pa Nkhani ya Kulankhulana Bwino UTUMIKI KOMANSO MOYO WATHU WACHIKHRISTU–NDANDANDA YA MISONKHANO Zimene Tikuphunzira pa Nkhani ya Kulankhulana Bwino Chinenero Chamanja cha ku Malawi Zimene Tikuphunzira pa Nkhani ya Kulankhulana Bwino https://cms-imgp.jw-cdn.org/img/p/202023326/univ/art/202023326_univ_sqr_xl.jpg mwb23.9 7