Phunzirani kwa Mphunzitsi Waluso

MUTU 10

Yesu Ali ndi Mphamvu Kuposa Ziwanda

Sitiyenera kuopa ziwanda komabe tiyenera kukhala osamala kuti zisatipusitse.

MUTU 32

Mmene Yesu Anatetezedwera

Phunzirani mmene Yehova anatetezera Yesu kwa anthu amene ankafuna kumupha ali mwana.