CHIGAWO 9 Kodi Paradaiso Adzabwera Liti? YAMBANI Kodi Paradaiso Adzabwera Liti? Pepani, zalephereka. Koperani Vidiyoyi Onetsani Kaonekedwe ka Mawu Bisani Kaonekedwe ka Mawu Mavuto amene akuchitika padzikoli akusonyeza kuti posachedwapa, Ufumu wa Mulungu uyamba kulamulira padziko lapansi. Luka 21:10, 11; 2 Timoteyo 3:1-5 Baibulo linaneneratu zinthu zambiri zimene zikuchitika masiku ano. Linaneneratu kuti anthu adzakhala okonda ndalama, osamvera makolo, oopsa ndiponso okonda zosangalatsa. Linanenanso kuti kudzakhala zivomezi zamphamvu, nkhondo, njala ndiponso miliri. Zinthu zimenezi zikuchitika masiku ano. Yesu ananenanso kuti uthenga wabwino wonena za Ufumu udzalalikidwa padziko lonse lapansi.—Mateyu 24:14. Ufumu umenewu udzachotsa zinthu zonse zoipa. 2 Petulo 3:13 Posachedwapa, Yehova awononga anthu oipa. Satana ndi ziwanda zake adzalangidwa. Anthu amene amamvera Mulungu adzapulumuka n’kulowa m’dziko latsopano lolungama. M’dziko limeneli anthu adzakhala mopanda mantha ndipo azidzakhulupirirana ndi kukondana kwambiri. Yam'mbuyo Yotsatira Mwina Mungakondenso Kudziwa Izi MABUKU Kodi Ufumu wa Mulungu N’chiyani? Pamene Yesu anali padziko lapansi, anasonyeza zimene Ufumuwo udzachitire anthu. MABUKU Kodi Mavuto Amene Tikukumana Nawowa Adzathadi? Baibulo limanena kuti Mulungu adzathetsa mavuto onse. Limanenanso kuti iye amadana ndi kupanda chilungamo ndipo amakonda anthu. Kodi zimenezi zikukukhudzani bwanji? Sindikizani Patsani ena Patsani ena Kodi Paradaiso Adzabwera Liti? MVERANI MULUNGU KUTI MUDZAPEZE MOYO WOSATHA Kodi Paradaiso Adzabwera Liti? Chinenero Chamanja cha ku Malawi Kodi Paradaiso Adzabwera Liti? https://assetsnffrgf-a.akamaihd.net/assets/ct/f62df3bf2a/images/syn_placeholder_sqr.png