CHIGAWO 12 Kodi Mungatani Kuti Aliyense M’banja Mwanu Azisangalala? YAMBANI Kodi Mungatani Kuti Aliyense M’banja Mwanu Azisangalala? Pepani, zalephereka. Koperani Vidiyoyi Onetsani Kaonekedwe ka Mawu Bisani Kaonekedwe ka Mawu Chikondi n’chofunika kwambiri kuti aliyense m’banja akhale wosangalala. Aefeso 5:33 Zimene Mulungu amafuna pa nkhani ya ukwati n’zakuti mwamuna akhale ndi mkazi mmodzi komanso mkazi akhale ndi mwamuna mmodzi. Mwamuna wachikondi amakomera mtima mkazi wake ndiponso amamumvetsa. Mkazi ayenera kuchita zinthu mogwirizana ndi mwamuna wake. Ana ayenera kumvera makolo awo. Khalani okoma mtima ndiponso okhulupirika, osati ankhanza. Akolose 3:5, 8-10 Mawu a Mulungu amanena kuti mwamuna azikonda mkazi wake ngati mmene amakondera thupi lake, ndiponso kuti mkazi azilemekeza kwambiri mwamuna wake. Kugonana ndi munthu amene si mkazi kapena mwamuna wanu n’kulakwa. Kukwatira mitala n’kulakwanso. Mawu a Yehova ali ndi mfundo zimene zingathandize mabanja kukhala osangalala. Yam'mbuyo Yotsatira Mwina Mungakondenso Kudziwa Izi MABUKU Kodi N’chiyani Chingathandize Kuti Banja Likhale Losangalala? Anthu ena amaganiza kuti ndalama zingachititse banja lawo kukhala losangalala. Koma kodi zimenezi n’zoona? Sindikizani Patsani ena Patsani ena Kodi Mungatani Kuti Aliyense M’banja Mwanu Azisangalala? MVERANI MULUNGU KUTI MUDZAPEZE MOYO WOSATHA Kodi Mungatani Kuti Aliyense M’banja Mwanu Azisangalala? Chinenero Chamanja cha ku Malawi Kodi Mungatani Kuti Aliyense M’banja Mwanu Azisangalala? https://assetsnffrgf-a.akamaihd.net/assets/ct/e781f8601f/images/syn_placeholder_sqr.png