Mfundo Zina Zothandiza Mabanja YAMBANI Mfundo Zina Zothandiza Mabanja Pepani, zalephereka. Koperani Vidiyoyi Onetsani Kaonekedwe ka Mawu Bisani Kaonekedwe ka Mawu BAIBULO LIMAPEREKA MALANGIZO OTHANDIZA KWAMBIRI kwa anthu okwatirana, makolo komanso kwa achinyamata. Malangizo ake angakuthandizeni kukhala oganiza bwino komanso kusankha bwino zochita.—Miyambo 1:1-4. BAIBULO LIMAYANKHANSO MAFUNSO OFUNIKA KWAMBIRI MONGA: Kodi cholinga cha moyo n’chiyani? Kodi Mulungu ndi amene amachititsa kuti tizivutika? Kodi chimachitika n’chiyani tikamwalira? Tikukulimbikitsani kuti mufufuze m’Baibulo mayankho a mafunso amenewa komanso ena. Onerani kavidiyo kakuti, N’chifukwa Chiyani Tiyenera Kuphunzira Baibulo? popanga sikani kachidindo aka kapena pitani pa www.pr418.com/ny. Yam'mbuyo Yotsatira Mwina Mungakondenso Kudziwa Izi MABUKU Banja Lanu Likhoza Kukhala Losangalala Mukhoza kukhala ndi banja losangalala mukamatsatira mfundo za m’Baibulo. Sindikizani Patsani ena Patsani ena Mfundo Zina Zothandiza Mabanja GALAMUKANI! Kuti Banja Liziyenda Bwino—Mfundo Zina Zothandiza Mabanja Chinenero Chamanja cha ku Malawi Kuti Banja Liziyenda Bwino—Mfundo Zina Zothandiza Mabanja https://cms-imgp.jw-cdn.org/img/p/102018057/univ/art/102018057_univ_sqr_xl.jpg g18.2 13