NSANJA YA OLONDA—YOPHUNZIRA February 2020
M’magaziniyi muli nkhani zophunzira kuyambira April 6–May 3, 2020.
Atate Wathu Yehova Amatikonda Kwambiri
Tisamakayikire kuti Atate wathu Yehova amatikonda komanso kutisamalira ndipo sangatisiye.
Timakonda Kwambiri Atate Wathu Yehova
Onani zinthu zimene tingachite posonyeza kuti timakonda kwambiri Atate wathu Yehova.
Muzipewa Nsanje Kuti Muzikhala Mwamtendere
Nthawi zina tikhoza kumavutika ndi mtima wa nsanje. Onani zimene tingachite kuti tipewe nsanje n’kumakhala mwamtendere ndi anzathu.
Muzilola Kuti Yehova Azikutonthozani
Hana, mtumwi Paulo ndi Mfumu Davide ankavutika ndi nkhawa. Kodi tingaphunzire chiyani tikaganizira mmene Yehova anawatonthozera?