NSANJA YA OLONDA—YOPHUNZIRA June 2017

M’magaziniyi muli nkhani zophunzira kuyambira pa July 31 mpaka August 27, 2017.

Yehova Amatitonthoza M’masautso Athu Onse

Kodi ndi mavuto ati amene Akhristu amakumana nawo m’banja masiku ano? Ngati mukukumana ndi mavuto amenewa kodi Mulungu angakulimbikitseni bwanji?

Tizikonda ndi Mtima Wonse Chuma Chimene Mulungu Watipatsa

Kodi ndi chuma chiti chimene tiyenera kuchikonda ndi mtima wonse ndipo tingachite bwanji zimenezi?

Musamaiwale Nkhani Yofunika Kwambiri

Kodi nkhani yofunika kwambiri ndi iti? Nanga n’chifukwa chiyani tiyenera kuikumbukira nthawi zonse?

Muzikhala Kumbali ya Ulamuliro wa Yehova

Kodi chimachitika n’chiyani munthu akazindikira mfundo yoti Yehova yekha ndi amene ali woyenera kulamulira chilengedwe chonse?