NSANJA YA OLONDA—YOPHUNZIRA March 2017

Magaziniyi ili ndi nkhani zophunzira kuyambira May 1 mpaka 28, 2017.

Tizipereka Ulemu kwa Oyenera Kulemekezedwa

Kodi tiyenera kupereka ulemu kwa ndani ndipo n’chifukwa chiyani? Kodi ubwino wopereka ulemu woyenera ndi wotani?

Muzikhulupirira Yehova Kuti Muzisankha Zochita Mwanzeru

Zinthu zina zimene timasankha, zimakhudza kwambiri moyo wathu. Ndiye tingatani kuti tizisankha zochita mwanzeru?

Tizitumikira Yehova ndi Mtima Wathunthu

Asa, Yehosafati, Hezekiya komanso Yosiya onsewa anali mafumu a Yuda ndipo analakwitsapo zinazake. Komabe Mulungu anawaona kuti ankamutumikira ndi mtima wathunthu. N’chifukwa chiyani zili choncho?

Kodi Mumatsatira ndi Mtima Wonse Zimene Zinalembedwa?

Tingaphunzire zambiri kuchokera pa zimene ena analakwitsa, ngakhalenso anthu otchulidwa m’Baibulo