NSANJA YA OLONDA—YOPHUNZIRA June 2018

M’magaziniyi muli nkhani zophunzira kuyambira pa August 6 mpaka pa September 2, 2018.

“Ufumu Wanga Suli Mbali ya Dziko Lino”

Kodi zimene Yesu ankachita popewa kukhala kumbali inayake pa nkhani zandale zingatithandize bwanji masiku ano?

Tonsefe Tikhale Ogwirizana Ngati Yehova ndi Yesu

Kodi tingalimbikitse bwanji mgwirizano m’gulu la Mulungu?

Muziphunzitsa Chikumbumtima Chanu ndi Malamulo Komanso Mfundo za Mulungu

Yehova anatipatsa chikumbumtima koma kuti tiyenera kuchiphunzitsa kuti chizititsogolera bwino.

“Onetsani Kuwala Kwanu” Kuti Yehova Alemekezeke

Pamafunika kuchita zambiri osati kungolalikira uthenga wabwino basi.