NSANJA YA OLONDA—YOPHUNZIRA July 2017

Muzifunafuna Chuma Chenicheni

Kodi tingagwiritse ntchito bwanji chuma chathu kuti tilimbitse ubwenzi wathu ndi Mulungu?

“Lirani ndi Anthu Amene Akulira”

Kodi n’chiyani chingalimbikitse munthu amene waferedwa? Nanga inuyo mungamuthandize bwanji?

N’chifukwa Chiyani Tiyenera Kutamanda Yehova?

Salimo 147 limatikumbutsa kuti tili ndi zifukwa zambiri zotichititsa kuyamikira ndiponso kuthokoza Mlengi wathu.

‘Mulungu Akwaniritse Zofuna Zanu’

Achinyamata ayenera kusankhiratu zimene adzachite m’tsogolo. Kuchita zimenezi kungakhale kovuta koma Yehova amadalitsa anthu amene amatsatira malangizo ake.