NSANJA YA OLONDA—YOPHUNZIRA October 2017

“Tizisonyezana Chikondi Chenicheni M’zochita Zathu”

Kodi tingasonyeze bwanji kuti tili ndi chikondi chenicheni osati chachinyengo?

Choonadi sichibweretsa “mtendere koma lupanga”

Kodi “lupanga” limene Yesu ananena kuti abweretsa n’chiyani, nanga lingakukhudzeni bwanji?

Kodi Masomphenya a Zekariya Akukukhudzani Bwanji?

N’chifukwa chiyani Mulungu anaonetsa Zekariya masomphenya a mpukutu ukuuluka, mkazi ali m’chiwiya komanso akazi awiri akuuluka?

Timatetezedwa ndi Magaleta Komanso Chisoti Chachifumu

Kodi masomphenya omaliza amene Zekariya anaona a mapiri amkuwa, magaleta okonzeka kupita kunkhondo ndiponso wansembe amene anapatsidwa ufumu akutsimikizira chiyani anthu a Mulungu masiku ano?