NSANJA YA OLONDA—YOPHUNZIRA March 2019

Chikundiletsa Kubatizidwa N’chiyani?

Anthu ena amene aphunzira za Yehova amaopa kubatizidwa. N’chiyani chingawathandize kuti alimbe mtima n’kubatizidwa?

Tizimvetsera Mawu a Yehova

Kodi Yehova amatilankhula bwanji masiku ano? Kodi kumvetsera Mawu a Mulungu kungatithandize bwanji?

Tizichita Zinthu Moganizira Ena

Kodi Yehova ndi Yesu amasonyeza bwanji kuti amaganizira ena? Nanga tingawatsanzire bwanji?

Tizisonyeza Anthu Chifundo Tikakhala mu Utumiki

Tchulani njira 4 zimene tingasonyezere kuti timaganizira ena mu utumiki.