NSANJA YA OLONDA—YOPHUNZIRA July 2019

Tizikonzekera Kuti Tidzathe Kupirira Pozunzidwa

Kodi tingatani kuti tikhale olimba mtima pokumana ndi anthu amene amadana nafe?

Tizilambirabe Yehova Ngakhale Boma Litatiletsa

Kodi tizitani ngati boma latiletsa kulambira Yehova?

‘Pitani Mukaphunzitse Anthu Kuti Akhale Ophunzira Anga’

N’chifukwa chiyani ntchito yothandiza anthu kukhala ophunzira a Khristu ndi yofunika kwambiri, nanga ndi zinthu ziti zimene zingatithandize pogwira ntchitoyi?

Kodi Tingathandize Bwanji Anthu Amene Sakonda Zachipembedzo?

Kodi tingathandize bwanji anthu amene sakonda zachipembedzo kuti azikonda Mulungu komanso kukhala ophunzira a Khristu?