NSANJA YA OLONDA—YOPHUNZIRA August 2019

“Sitikubwerera M’mbuyo”

Kodi zimene tikuyembekezera m’tsogolo zingatithandize bwanji kuti tisabwerere m’mbuyo?

Chikondi Chanu Chipitirire Kukula

Kalata yopita kumpingo wa Afilipi imatithandiza kudziwa zimene tingachite kuti chikondi chathu chipitirire kukula ngakhale titakumana ndi mavuto.

“Anthu Okumvera” Adzapulumuka

Kodi tingathandize bwanji achibale athu kuti aphunzire za Yehova?

Zimene Tingachite Kuti Tizisangalalabe Utumiki Wathu Ukasintha

Akhristu ambiri amavutika kusiya utumiki umene ankakonda kwambiri. N’chiyani chingawathandize kuzolowera utumiki watsopano?