NSANJA YA OLONDA—YOPHUNZIRA December 2019

Pali Nthawi Yogwira Ntchito ndi Nthawi Yopuma

Nkhaniyi itithandiza kukhala ndi maganizo oyenera pa nkhani ya ntchito ndi kupuma ndipo chitsanzo chake ndi cha lamulo la Sabata limene Aisiraeli anapatsidwa.

Yehova Anakonza Zoti Tikhale ndi Ufulu

Chaka cha Ufulu chimatikumbutsa zimene Yehova anakonza zoti tikhale ndi ufulu.

Kodi Mumamudziwa Bwino Yehova?

Kodi kumudziwa Yehova n’kutani, nanga tingaphunzire chiyani kwa Mose ndi Mfumu Davide pa nkhani yokhala pa ubwenzi wolimba ndi Yehova?

Makolo Ayenera Kuphunzitsa Ana Awo Kukonda Yehova

Kodi makolo angaphunzitse bwanji ana awo kuti azikonda Yehova komanso kumutumikira?