NSANJA YA OLONDA Na. 4 2016

NKHANI YAPACHIKUTO

Kodi Kudziwa Mmene Baibulo Linapulumukira N’kothandiza?

Palibe buku lina lililonse la chipembedzo lomwe lakhala likuthandiza anthu kuti azikhulupirira zinthu zolondola. Kodi Baibulo tingalikhulupirire?

NKHANI YAPACHIKUTO

Baibulo Linasungidwa Bwino Kuti Lisawole

Anthu omwe analemba komanso kukopera Baibulo ankagwiritsa ntchito mipukutu yopangidwa ndi gumbwa komanso zikopa. Kodi zinatheka bwanji kuti mipukutu yambiri ya Baibulo ifike masiku ano?

NKHANI YAPACHIKUTO

Baibulo Linasungidwa Ngakhale Kuti Ena Ankalitsutsa

Atsogoleri andale komanso azipembedzo akhala akuletsa anthu kumasulira, kusindikiza ngakhalenso kukhala ndi Baibulo, koma sizinatheke.

NKHANI YAPACHIKUTO

Baibulo Linapulumuka Ngakhale Kuti Ena Ankafuna Kusintha Uthenga Wake

Anthu amaganizo olakwika ankafuna kusintha uthenga wa m’Baibulo. Koma zolinga zawozi zinadziwika ndiponso zinalephereka?

NKHANI YAPACHIKUTO

N’chifukwa Chiyani Baibulo Linapulumuka

Kodi Baibulo ndi losiyana bwanji ndi mabuku ena?

THE BIBLE CHANGES LIVES

Ndinasintha Khalidwe Langa Movutikira Kwambiri

Kodi munthu wina anapeza bwanji mtendere wamumtima atasiya khalidwe loonera zolaula?