NSANJA YA OLONDA Na. 1 2017
NKHANI YAPACHIKUTO
Kodi Ubwino Wowerenga Baibulo Ndi Wotani?
Kodi anthu ambiri apindula bwanji ndi kuwerenga Baibulo?
NKHANI YAPACHIKUTO
Kodi Ndingayambe Bwanji?
Pali zinthu 5 zimene zingakuthandizeni kusangalala powerenga Baibulo.
NKHANI YAPACHIKUTO
Kodi Mungatani Kuti Kuwerenga Baibulo Kukhale Kosangalatsa?
Kuwerenga Baibulo kungakhale kosangalatsa mukamawerenga Baibulo labwino, mukamagwiritsa ntchito zipangizo zamakono ndiponso zinthu zothandiza kuphunzira komanso mukamatsatira njira zosiyanasiyana.
NKHANI YAPACHIKUTO
Kodi Baibulo Lingakuthandizeni Bwanji?
Buku lakaleli lili ndi malangizo anzeru kwambiri.
THE BIBLE CHANGES LIVES
Sindinkafuna Kufa
Yvonne Quarrie ankafuna kudziwa cholinga chimene Mulungu anamulengera. Yankho la funsoli linamuthandiza kuti asinthe moyo wake.