NSANJA YA OLONDA Na. 1 2017

NKHANI YAPACHIKUTO

Kodi Ubwino Wowerenga Baibulo Ndi Wotani?

Kodi anthu ambiri apindula bwanji ndi kuwerenga Baibulo?

NKHANI YAPACHIKUTO

Kodi Ndingayambe Bwanji?

Pali zinthu 5 zimene zingakuthandizeni kusangalala powerenga Baibulo.

NKHANI YAPACHIKUTO

Kodi Mungatani Kuti Kuwerenga Baibulo Kukhale Kosangalatsa?

Kuwerenga Baibulo kungakhale kosangalatsa mukamawerenga Baibulo labwino, mukamagwiritsa ntchito zipangizo zamakono ndiponso zinthu zothandiza kuphunzira komanso mukamatsatira njira zosiyanasiyana.

NKHANI YAPACHIKUTO

Kodi Baibulo Lingakuthandizeni Bwanji?

Buku lakaleli lili ndi malangizo anzeru kwambiri.

THE BIBLE CHANGES LIVES

Sindinkafuna Kufa

Yvonne Quarrie ankafuna kudziwa cholinga chimene Mulungu anamulengera. Yankho la funsoli linamuthandiza kuti asinthe moyo wake.