Pitani ku nkhani yake # link, for screen reader ##

Pitani ku mitu ya nkhani

Mfundo Zothandiza Kumvetsa Buku la Nahumu

Mfundo Zothandiza Kumvetsa Buku la Nahumu

Onerani vidiyoyi kuti mudziwe mfundo zachidule zokhudza buku la Nahumu. Bukuli limafotokoza ulosi umene umasonyeza kuti Yehova amachita zonse zimene wanena komanso kuti amadana ndi chiwawa.