NYIMBO 122 Khalani Olimba Komanso Osasunthika Sankhani Zoti Mumvetsere Khalani Olimba Komanso Osasunthika Pepani, zalephereka. Koperani Vidiyoyi Onetsani Kaonekedwe ka Mawu Bisani Kaonekedwe ka Mawu Kukula kwa Zilembo Chithunzi (1 Akorinto 15:58) 1. Anthu akuvutika kwambiri Ndipo akuopa zam’tsogolo. Ife tilimbe tisasunthike Potumikira M’lungu. (KOLASI) Tiyenera kulimba. Tisiyane ndi dziko. Tikhale olimba. Tidzapeza moyo. 2. Misampha ndi yambiri m’dzikoli Koma tingaipewe mwanzeru. Tikamadanatu ndi zoipa Sitidzasunthikadi. (KOLASI) Tiyenera kulimba. Tisiyane ndi dziko. Tikhale olimba. Tidzapeza moyo. 3. Tizilambira Yehova yekha. Tim’tumikire ndi mtima wonse. Tizilalikiradi mwakhama. Mapeto akubwera. (KOLASI) Tiyenera kulimba. Tisiyane ndi dziko. Tikhale olimba. Tidzapeza moyo. (Onaninso Luka 21:9; 1 Pet. 4:7.) Yam'mbuyo Yotsatira Sindikizani Patsani ena Patsani ena Khalani Olimba Komanso Osasunthika IMBIRANI YEHOVA MOSANGALALA Khalani Olimba Komanso Osasunthika (Nyimbo 122) Chinenero Chamanja cha ku Malawi Khalani Olimba Komanso Osasunthika (Nyimbo 122) https://cms-imgp.jw-cdn.org/img/p/1102016922/sign/wpub/1102016922_sign_sqr_xl.jpg sjj 122