NYIMBO 151 Iye Adzaitana Sankhani Zoti Mumvetsere Iye Adzaitana Pepani, zalephereka. Koperani Vidiyoyi Onetsani Kaonekedwe ka Mawu Bisani Kaonekedwe ka Mawu Kukula kwa Zilembo Chithunzi (Yobu 14:13-15) 1. Moyo wathu sumachedwa kutha, Timafadi mwamsanga. Mukanthawi kochepa kwambiri, Timayamba kulira. Kodi akufa angadzukenso? M’lungu akulonjeza: (KOLASI) Iye adzawaitana; Akufa adzayankha. Ntchito ya manja ake. Adzailakalaka. Inu musakayikire, M’lungu adzatidzutsa. Tidzakhala kosatha, Mongadi anthu ake. 2. Anthu a M’lungu akamwalira, Iye sawaiwala. Omwe amawakumbukiratu, Iye adzawadzutsa. Ndipo tonse tidzasangalala Ndi moyo m’paradaiso. (KOLASI) Iye adzawaitana; Akufa adzayankha. Ntchito ya manja ake. Adzailakalaka. Inu musakayikire, M’lungu adzatidzutsa. Tidzakhala kosatha, Mongadi anthu ake. (Onaninso Yoh. 6:40; 11:11, 43; Yak. 4:14.) Yam'mbuyo Yotsatira Sindikizani Patsani ena Patsani ena Iye Adzaitana IMBIRANI YEHOVA MOSANGALALA Iye Adzaitana (Nyimbo 151) Chinenero Chamanja cha ku Malawi Iye Adzaitana (Nyimbo 151) https://assetsnffrgf-a.akamaihd.net/assets/ct/e781f8601f/images/syn_placeholder_sqr.png sjj song 151