NYIMBO 25 Chuma Chapadera Sankhani Zoti Mumvetsere Chuma Chapadera Pepani, zalephereka. Koperani Vidiyoyi Onetsani Kaonekedwe ka Mawu Bisani Kaonekedwe ka Mawu Kukula kwa Zilembo Chithunzi (1 Petulo 2:9) 1. Odzozedwa ndi mtundu, Watsopano wa M’lungu. Iye anawagula, Padziko lapansi. (KOLASI) N’chuma chapadera, Otchedwa dzina lanu Amakukondani. Amalengezadi za inu. 2. Ndi mtundu woyeradi, Wophunzitsa cho’nadi. Mulungu wawapatsa Kuwala kwakedi. (KOLASI) N’chuma chapadera, Otchedwa dzina lanu Amakukondani. Amalengezadi za inu. 3. Amasonkhanitsanso, Nkhosa zina mwakhama. Ndi okhulupirika. Kwa Mwanawankhosa. (KOLASI) N’chuma chapadera, Otchedwa dzina lanu Amakukondani. Amalengezadi za inu. (Onaninso Yes. 43:20b, 21; Mal. 3:17; Akol. 1:13.) Yam'mbuyo Yotsatira Sindikizani Patsani ena Patsani ena Chuma Chapadera IMBIRANI YEHOVA MOSANGALALA Chuma Chapadera (Nyimbo 25) Chinenero Chamanja cha ku Malawi Chuma Chapadera (Nyimbo 25) https://cms-imgp.jw-cdn.org/img/p/1102016825/sign/wpub/1102016825_sign_sqr_xl.jpg sjj 25