NYIMBO 49 Tizikondweretsa Mtima wa Yehova Sankhani Zoti Mumvetsere Tizikondweretsa Mtima wa Yehova Pepani, zalephereka. Koperani Vidiyoyi Onetsani Kaonekedwe ka Mawu Bisani Kaonekedwe ka Mawu Kukula kwa Zilembo Chithunzi (Miyambo 27:11) 1. M’lungu takulonjezani; Kuchita zofuna zanu, Tidzagwira ntchito yanu Mtima wanu ukondwere. 2. Kapolo wanu padziko, Amalengeza za inu Amatipatsa chakudya, Kuti tizikumverani. 3. Mutipatse mzimu wanu, Kuti tikhulupirike Ndipo tibale zipatso. Tizikusangalatsani. (Onaninso Mat. 24:45-47; Luka 11:13; 22:42.) Yam'mbuyo Yotsatira Sindikizani Patsani ena Patsani ena Tizikondweretsa Mtima wa Yehova IMBIRANI YEHOVA MOSANGALALA Tizikondweretsa Mtima wa Yehova (Nyimbo 49) Chinenero Chamanja cha ku Malawi Tizikondweretsa Mtima wa Yehova (Nyimbo 49) https://cms-imgp.jw-cdn.org/img/p/1102016849/sign/wpub/1102016849_sign_sqr_xl.jpg sjj 49