NYIMBO 60

Akamvera Adzapeza Moyo

Akamvera Adzapeza Moyo

(Ezekieli 3:17-19)

  1. 1. Mulungu akufuna

    tichenjeze anthu

    Kuti tsiku la mkwiyo

    wake likubwera.

    (KOLASI)

    Akamvera adzapeza,

    Inde moyo wosatha.

    Nafe tidzapulumuka,

    Tikafalitsa uthenga,

    Uthenga.

  2. 2. Tili ndi uthenga

    woti tiuze anthu.

    Tiitane anthu abwere

    kwa Mulungu.

    (KOLASI)

    Akamvera adzapeza,

    Inde moyo wosatha.

    Nafe tidzapulumuka,

    Tikafalitsa uthenga,

    Uthenga.

    (VESI LOKOMETSERA)

    Mwamsanga tilengeze,

    Anthu amve, aphunzire.

    Cho’nadi tiphunzitse,

    Kuti moyo adzapeze.

    (KOLASI)

    Akamvera adzapeza,

    Inde moyo wosatha.

    Nafe tidzapulumuka,

    Tikafalitsa uthenga,

    Uthenga.