NYIMBO 86 Tikhale Anthu Ophunzitsidwa Sankhani Zoti Mumvetsere Tikhale Anthu Ophunzitsidwa Pepani, zalephereka. Koperani Vidiyoyi Onetsani Kaonekedwe ka Mawu Bisani Kaonekedwe ka Mawu Kukula kwa Zilembo Chithunzi (Yesaya 50:4; 54:13) 1. Bwerani mosangalala muphunzire. “Bwerani m’dzamwe madzi a moyo.” Dzadyeni inu nonse anjala. Mudzalandiretu malangizo. 2. Tisaleketu kusonkhana pamodzi, Tiziphunzitsidwa ndi Mulungu. Kuno n’kumene kuli abale, Kuno kulitu mzimu wa M’lungu. 3. Lilime lophunzitsidwa choonadi. N’losangalatsa kulimvetsera, Tipezeke ndi anthu a M’lungu, Tizipezeka pamisonkhano. (Onaninso Aheb. 10:24, 25; Chiv. 22:17.) Yam'mbuyo Yotsatira Sindikizani Patsani ena Patsani ena Tikhale Anthu Ophunzitsidwa IMBIRANI YEHOVA MOSANGALALA Tikhale Anthu Ophunzitsidwa (Nyimbo 86) Chinenero Chamanja cha ku Malawi Tikhale Anthu Ophunzitsidwa (Nyimbo 86) https://cms-imgp.jw-cdn.org/img/p/1102016886/sign/wpub/1102016886_sign_sqr_xl.jpg sjj 86