Chikondi Sichitha YAMBANI Chikondi Sichitha Pepani, zalephereka. Koperani Vidiyoyi Onetsani Kaonekedwe ka Mawu Bisani Kaonekedwe ka Mawu Kukula kwa Zilembo Chithunzi (1 Akorinto 13:8) Pangani Dawunilodi: Manotsi 1. Tangoonani; Timakondanadi— Zomwe n’zosowa m’dzikoli. Ndi anzathuwa Tikusangalala, Sitili mbali ya dziko. (KUKONZEKERA KOLASI) Chikondi sichithadi. Chimapiriratu. (KOLASI) Chikondichitu— Yehova n’chikondi. Watipatsa. Chikondichitu— Ndi chofunikadi. Tizikondanabe, Ndipo tisasiye— Chikondichi. 2. Pena mavuto Angatifo’ketse N’kuvutika kupirira, Koma kupatsa Ndi kosangalatsa, M’lungu amatitonthoza. (KUKONZEKERA KOLASI) Chikondi sichithadi. Chimapiriratu. (KOLASI) Chikondichitu— Yehova n’chikondi. Watipatsa. Chikondichitu— Ndi chofunikadi. Tizikondanabe, Ndipo tisasiye. (KOLASI) Chikondichitu— Yehova n’chikondi. Watipatsa. Chikondichitu— Ndi chofunikadi. Tizikondanabe, Ndipo tisasiye— Chikondichi, Chikondichi, Chikondichi. Yam'mbuyo Yotsatira Sindikizani Patsani ena Patsani ena Chikondi Sichitha NYIMBO ZATHU Chikondi Sichitha Chinenero Chamanja cha ku Malawi Chikondi Sichitha https://cms-imgp.jw-cdn.org/img/p/1014320/univ/art/1014320_univ_sqr_xl.jpg