Ndithandizeni Ndikhale Wolimba Mtima YAMBANI Ndithandizeni Ndikhale Wolimba Mtima Pepani, zalephereka. Koperani Vidiyoyi Onetsani Kaonekedwe ka Mawu Bisani Kaonekedwe ka Mawu (2 Mafumu 6:16) Pangani Dawunilodi: Manotsi 1. Ndilitu ndi mantha— Zinthu zikuvuta. M’mavuto m’mandithandiza; M’makhala pafupi. Ndingavutikedi, Koma ndikudziwa: Ndinu wokhulupirika, Mudzanditeteza. (KOLASI) Yehova, mundithandize Ndiziona kuti Ndizothekatu kupirira Ndilimbedi mtima. Tili ndi ambiri Kuposa ’daniwa. Yehova thandizeni; Muwagonjetsadi. 2. Ndingachite mantha. Pandekha n’zovuta. Mumanditeteza ndithu; Ndidalire inu. Mundithandizetu, Ndisachite mantha. Palibe choti ndiope, M’ndende kaya imfa. (KOLASI) Yehova, mundithandize Ndiziona kuti Ndizothekatu kupirira. Ndilimbedi mtima. Tili ndi ambiri; Kuposa ’daniwa. Yehova thandizeni; Muwagonjetsadi. (KOLASI) Yehova, mundithandize Ndiziona kuti Ndizothekatu kupirira. Ndilimbedi mtima. Tili ndi ambiri; Kuposa ’daniwa. Yehova thandizeni; Muwagonjetsadi. Yehova thandizeni; Muwagonjetsadi. Yam'mbuyo Yotsatira Sindikizani Patsani ena Patsani ena Ndithandizeni Ndikhale Wolimba Mtima Ndithandizeni Ndikhale Wolimba Mtima Chinenero Chamanja cha ku Malawi Ndithandizeni Ndikhale Wolimba Mtima https://cms-imgp.jw-cdn.org/img/p/1014269/univ/art/1014269_univ_sqr_xl.jpg