Tili M’banja la Yehova YAMBANI Tili M’banja la Yehova Pepani, zalephereka. Koperani Vidiyoyi Onetsani Kaonekedwe ka Mawu Bisani Kaonekedwe ka Mawu 1. M’dzikoli anthu anaipa, Moti sizophweka kupeza mabwenzi. Ndinkafunitsitsa n’tapeza anzanga Odalirika ndi ondikondadi. 2. Lero ndawapeza, ndakhutira. Gulutu la Yehova lero ndalipeza. Anthu ake onse amakondana, N’zosangalatsa, ndapeza gulu labwino. (VESI LOKOMETSERA) Ndapeza ’bale ndi alongo, ndi makolonso. Ndapezatu anzanga osangalatsa Ochokera m’mitundu ndi mayiko onse. Timakondana, ndife banja limodzi. 3. Timadziwika ndi chikondi. M’gulu lapaderali timasangalala. Ndiye tikamakondana kwambiri Mulungu wathu amasangalaladi. (VESI LOKOMETSERA) Tachokera m’mayiko ndi mitundu yonse. Timakondana, ndife banja limodzi. 4. Tilitu m’gulu lapaderali, Yehova watikoka, n’zosangalatsadi. Tidzalowatu m’dziko latsopano Mongadi banja la padzikotu lonse. Monga banjatu limodzidi, Limodzi, Limodzi. Yam'mbuyo Yotsatira Sindikizani Patsani ena Patsani ena Tili M’banja la Yehova NYIMBO ZATHU Tili M’banja la Yehova Chinenero Chamanja cha ku Malawi Tili M’banja la Yehova https://cms-imgp.jw-cdn.org/img/p/1014348/univ/wpub/1014348_univ_sqr_xl.jpg