FEBRUARY 1, 2021 ERITREA A Mboni za Yehova Enanso Atatu Atulutsidwa M’ndende ku Eritrea YAMBANI A Mboni za Yehova Enanso Atatu Atulutsidwa M’ndende ku Eritrea Pepani, zalephereka. Koperani Vidiyoyi Onetsani Kaonekedwe ka Mawu Bisani Kaonekedwe ka Mawu Pa 1 February 2021, akuluakulu a boma ku Eritrea anatulutsa m’ndende m’bale mmodzi ndi alongo awiri. Iwo akhala m’ndende kuyambira zaka 4 mpaka 9 chifukwa chotsatira zimene amakhulupirira. Tikupitiriza kupempherera abale ndi alongo 20 omwe adakali m’ndende omwe akupitirizabe kukhala okhulupirika kwa Yehova.—2 Akorinto 1:11. Sindikizani Patsani ena Patsani ena A Mboni za Yehova Enanso Atatu Atulutsidwa M’ndende ku Eritrea NKHANI A Mboni za Yehova Enanso Atatu Atulutsidwa M’ndende ku Eritrea Chinenero Chamanja cha ku Malawi A Mboni za Yehova Enanso Atatu Atulutsidwa M’ndende ku Eritrea https://assetsnffrgf-a.akamaihd.net/assets/ct/f62df3bf2a/images/syn_placeholder_sqr.png